Luka 6:46 - Buku Lopatulika46 Ndipo munditchuliranji Ine, Ambuye, Ambuye, ndi kusachita zimene ndizinena? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201446 Ndipo munditchuliranji Ine, Ambuye, Ambuye, ndi kusachita zimene ndizinena? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa46 “Bwanji mumangoti, ‘Ambuye, Ambuye,’ koma chonsecho simuchita zimene ndimanena? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero46 “Kodi nʼchifukwa chiyani munditchula kuti, ‘Ambuye, Ambuye’ koma simuchita zimene Ine ndinena? Onani mutuwo |