Luka 6:40 - Buku Lopatulika40 Wophunzira saposa mphunzitsi wake; koma yense, m'mene atakonzedwa mtima, adzafanana ndi mphunzitsi wake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201440 Wophunzira saposa mphunzitsi wake; koma yense, m'mene atakonzedwa mtima, adzafanana ndi mphunzitsi wake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa40 Wophunzira saposa mphunzitsi wake, koma aliyense pamene watsiriza maphunziro ake, adzafanafana ndi mphunzitsi wake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero40 Wophunzira sangapose mphunzitsi wake, koma yense amene waphunzitsidwa bwinobwino adzakhala ngati mphunzitsi wake. Onani mutuwo |