Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 6:32 - Buku Lopatulika

32 Ndipo ngati muwakonda iwo akukondana ndinu, mudzalandira chiyamiko chotani? Pakuti ochimwa omwe akonda iwo akukondana nao.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

32 Ndipo ngati muwakonda iwo akukondana ndinu, mudzalandira chiyamiko chotani? Pakuti ochimwa omwe akonda iwo akukondana nao.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

32 “Ngati mukonda okhawo amene amakukondani, mungayembekeze kulandira mphotho yanji? Pajatu ngakhale anthu ochimwa amakondanso amene amaŵakonda.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

32 “Ngati mukonda okhawo amene amakukondani, mwapindula chiyani? Ngakhale ‘ochimwa’ amakonda amene amawakondanso.

Onani mutuwo Koperani




Luka 6:32
3 Mawu Ofanana  

Ndipo ngati muwachitira zabwino iwo amene akuchitirani inu zabwino, mudzalandira chiyamiko chotani? Pakuti anthu ochimwa omwe amachita chomwecho.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa