Luka 6:27 - Buku Lopatulika27 Koma ndinena kwa inu akumva, Kondanani nao adani anu; chitirani zabwino iwo akuda inu, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201427 Koma ndinena kwa inu akumva, Kondanani nao adani anu; chitirani zabwino iwo akuda inu, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa27 “Koma inu amene mukumva mau anga, ndikukuuzani kuti, Muzikonda adani anu, muziŵachitira zabwino amene amadana nanu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero27 “Koma Ine ndikuwuza inu amene mukundimva: Kondani adani anu, chitirani zabwino amene amakudani. Onani mutuwo |