Luka 6:2 - Buku Lopatulika2 Koma Afarisi ena anati, Muchitiranji chosaloledwa kuchitika tsiku la Sabata? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Koma Afarisi ena anati, Muchitiranji chosaloledwa kuchitika tsiku la Sabata? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Apo Afarisi ena adafunsa kuti, “Bwanji mukuchita zimene siziloledwa pa tsiku la Sabata?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Ena mwa Afarisi anafunsa kuti, “Kodi nʼchifukwa chiyani mukuchita zosaloledwa pa tsiku la Sabata?” Onani mutuwo |