Luka 5:38 - Buku Lopatulika38 Koma kuyenera kutsanulira vinyo watsopano m'matumba atsopano. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201438 Koma kuyenera kutsanulira vinyo watsopano m'matumba atsopano. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa38 Koma vinyo watsopano amamuthira m'matumba atsopanonso. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero38 Ayi, vinyo watsopano ayenera kuthiridwa mʼmatumba a vinyo azikopa zatsopano. Onani mutuwo |