Luka 5:39 - Buku Lopatulika39 Ndipo palibe munthu atamwa vinyo wakale afuna watsopano; pakuti anena, Wakale ali wokoma. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201439 Ndipo palibe munthu atamwa vinyo wakale afuna watsopano; pakuti anena, Wakale ali wokoma. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa39 “Ndipo munthu akangolaŵa vinyo wakale, watsopano sangamufune. Pajatu amati, ‘Wakale ndiye vinyo chaiye.’ ” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero39 Ndipo palibe amene atamwa vinyo wakale amafuna watsopano, pakuti amati, ‘Wakale ndi okoma.’ ” Onani mutuwo |