Luka 5:32 - Buku Lopatulika32 Sindinadza Ine kuitana olungama, koma ochimwa kuti atembenuke mtima. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201432 Sindinadza Ine kuitana olungama, koma ochimwa kuti atembenuke mtima. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa32 Inetu sindidabwere kudzaitana anthu olungama, koma anthu ochimwa, kuti atembenuke mtima.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero32 Ine sindinabwere kudzayitana olungama, koma ochimwa kuti atembenuke mtima.” Onani mutuwo |