Luka 5:22 - Buku Lopatulika22 Koma Yesu anadziwa zoyesayesa zao, nayankha, nati kwa iwo, Muyesayesa bwanji m'mitima yanu? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Koma Yesu anadziwa zoyesayesa zao, nayankha, nati kwa iwo, Muyesayesa bwanji m'mitima yanu? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Yesu adaadziŵa maganizo ao, ndiye adaŵafunsa kuti, “Bwanji mukuganiza zimenezo mumtima mwanu? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Yesu anadziwa zomwe iwo amaganiza ndipo anafunsa kuti, “Kodi ndi chifukwa chiyani mukuganiza zimenezi mʼmitima mwanu? Onani mutuwo |