Luka 5:2 - Buku Lopatulika2 ndipo anaona ngalawa ziwiri zinakhala m'mbali mwa nyanja; koma asodzi a nsomba adatuluka m'menemo, nalikutsuka makoka ao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 ndipo anaona ngalawa ziwiri zinakhala m'mbali mwa nyanja; koma asodzi a nsomba adatuluka m'menemo, nalikutsuka makoka ao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Iye adaona zombo ziŵiri pamphepetepo. Asodzi anali atatulukamo, ndipo ankatsuka makoka ao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Iye anaona mabwato awiri ali mʼmphepete mwa nyanja, asodzi amene ankachapa makhoka awo atawasiya pamenepo. Onani mutuwo |