Luka 5:16 - Buku Lopatulika16 Koma Iye anazemba, nanka m'mapululu, nakapemphera. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Koma Iye anazemba, nanka m'mapululu, nakapemphera. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Koma Iye adapita kumalo kosapitapita anthu, namakapemphera kumeneko. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Koma Yesu nthawi zambiri ankachoka kupita ku malo a yekha kukapemphera. Onani mutuwo |