Luka 4:7 - Buku Lopatulika7 Chifukwa chake ngati Inu mudzagwadira pamaso panga, wonsewo udzakhala wanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Chifukwa chake ngati Inu mudzagwadira pamaso panga, wonsewo udzakhala wanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Choncho mukandipembedza, zonsezi zidzakhala zanu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Ngati mutandilambira, zonsezi zidzakhala zanu.” Onani mutuwo |