Luka 4:37 - Buku Lopatulika37 Ndipo mbiri yake ya Iye inafalikira kumalo onse a dziko loyandikira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201437 Ndipo mbiri yake ya Iye inafalikira kumalo onse a dziko loyandikira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa37 Motero mbiri ya Yesu idawanda ku dera lonselo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero37 Ndipo mbiri yake inafalikira madera onse ozungulira. Onani mutuwo |