Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 4:37 - Buku Lopatulika

37 Ndipo mbiri yake ya Iye inafalikira kumalo onse a dziko loyandikira.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

37 Ndipo mbiri yake ya Iye inafalikira kumalo onse a dziko loyandikira.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

37 Motero mbiri ya Yesu idawanda ku dera lonselo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

37 Ndipo mbiri yake inafalikira madera onse ozungulira.

Onani mutuwo Koperani




Luka 4:37
8 Mawu Ofanana  

Taonani, Mtumiki wanga adzachita mwanzeru; adzakwezedwa ndi kutukulidwa pamwamba, nadzakhala pamwambamwamba.


Ndipo mbiri yake imene inabuka m'dziko lonse limenelo.


Koma iwo anatulukamo, nabukitsa mbiri yake m'dziko lonselo.


Ndipo mbiri yake inabuka pompaja kudziko lonse la Galileya lozungulirapo.


Koma iye anatuluka nayamba kulalikira ndithu, ndi kubukitsa mauwo, kotero kuti Yesu sanathe kulowanso poyera m'mudzi, koma anakhala padera m'mapululu; ndipo anadza kwa Iye anthu a kumalo onse.


Ndipo mfumu Herode anamva izi; pakuti dzina lake lidamveka; ndipo ananena, kuti, Yohane Mbatizi wauka kwa akufa, ndipo chifukwa chake mphamvu izi zichitachita mwa Iye.


Ndipo Yesu anabwera ndi mphamvu ya Mzimu ku Galileya; ndipo mbiri yake ya Iye inabuka ku dziko lonse loyandikira.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa