Luka 4:28 - Buku Lopatulika28 Ndipo onse a m'sunagogemo anadzala ndi mkwiyo pakumva izi; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201428 Ndipo onse a m'sunagogemo anadzala ndi mkwiyo pakumva izi; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa28 Anthu onse amene anali m'nyumba yamapemphero muja atamva mau ameneŵa, adapsa mtima kwambiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero28 Anthu onse mʼsunagogemo anapsa mtima atamva izi. Onani mutuwo |