Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 4:28 - Buku Lopatulika

28 Ndipo onse a m'sunagogemo anadzala ndi mkwiyo pakumva izi;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

28 Ndipo onse a m'sunagogemo anadzala ndi mkwiyo pakumva izi;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

28 Anthu onse amene anali m'nyumba yamapemphero muja atamva mau ameneŵa, adapsa mtima kwambiri.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

28 Anthu onse mʼsunagogemo anapsa mtima atamva izi.

Onani mutuwo Koperani




Luka 4:28
13 Mawu Ofanana  

Koma Asa anakwiya naye mlauliyo, namuika m'kaidi; pakuti adapsa naye mtima chifukwa cha ichi. Nthawi yomweyi Asa anasautsa anthu ena.


Ndipo anatenga Yeremiya, namponya iye m'dzenje la Malikiya mwana wake wa mfumu, limene linali m'bwalo la kaidi; ndipo anamtsitsa Yeremiya ndi zingwe. Koma m'dzenjemo munalibe madzi, koma thope; namira Yeremiya m'thopemo.


Pamenepo Herode, poona kuti anampusitsa Anzeruwo, anapsa mtima ndithu, natumiza ena kukaononga tiana tonse ta mu Betelehemu ndi ta m'midzi yake yonse, takufikira zaka ziwiri ndi tating'ono tonse, monga mwa nthawi imeneyo iye anafunsitsa kwa Anzeruwo.


Ndipo munali akhate ambiri mu Israele masiku a Elisa mneneri; ndipo palibe mmodzi wa iwo anakonzedwa, koma Naamani yekha wa ku Siriya.


nanyamuka namtulutsira Iye kunja kwa mzindawo, nanka naye pamutu paphiri pamene panamangidwa mzinda wao, kuti akamponye Iye pansi.


Koma iwowo anagwidwa misala; nalankhulana wina ndi mnzake kuti amchitire Yesu chiyani.


Koma m'mene anamva iwo analaswa mtima, nafuna kuwapha.


Koma pakumva izi analaswa mtima, namkukutira mano.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa