Luka 4:24 - Buku Lopatulika24 Ndipo Iye anati, Indetu, ndinena kwa inu, kuti, Palibe mneneri alandirika kudziko la kwao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 Ndipo Iye anati, Indetu, ndinena kwa inu, kuti, Palibe mneneri alandirika kudziko la kwao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 Adaŵauzanso kuti, “Ndithu ndikunenetsa kuti palibe mneneri amene amalandiridwa bwino kumudzi kwao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 Iye anapitiriza kuti, “Zoonadi, ndikukuwuzani kuti palibe mneneri amene amavomerezedwa ku mudzi kwawo. Onani mutuwo |