Luka 4:2 - Buku Lopatulika2 kukayesedwa ndi mdierekezi masiku makumi anai. Ndipo Iye sanadye kanthu masiku awo; ndipo pamene anatha anamva njala. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 kukayesedwa ndi mdierekezi masiku makumi anai. Ndipo Iye sanadye kanthu masiku awo; ndipo pamene anatha anamva njala. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 masiku makumi anai, ndipo kumeneko Satana ankamuyesa. Yesu sankadya kanthu masiku amenewo, ndipo pamene masikuwo adatha, adamva njala. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 kumene anayesedwa ndi mdierekezi masiku makumi anayi. Sanadye kena kalikonse pa masiku amenewo, ndipo pa mapeto pake anamva njala. Onani mutuwo |