Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 3:6 - Buku Lopatulika

6 ndipo anthu onse adzaona chipulumutso cha Mulungu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 ndipo anthu onse adzaona chipulumutso cha Mulungu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 Motero anthu onse adzaona chipulumutso chochokera kwa Mulungu.’ ”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 Ndipo anthu onse adzaona chipulumutso cha Mulungu.”

Onani mutuwo Koperani




Luka 3:6
9 Mawu Ofanana  

ndipo ulemerero wa Yehova udzavumbulutsidwa, ndipo anthu onse adzauona pamodzi, pakuti pakamwa pa Yehova panena chomwecho.


inde, ati, Chili chinthu chopepuka ndithu kuti Iwe ukhale mtumiki wanga wakuutsa mafuko a Yakobo, ndi kubwezera osungika a Israele; ndidzakupatsanso ukhale kuunika kwa amitundu, kuti ukhale chipulumutso changa mpaka ku malekezero a dziko lapansi.


Yehova wavula mkono wake woyera pamaso pa amitundu onse; ndi malekezero onse a dziko lapansi adzaona chipulumutso cha Mulungu wathu.


Ndipo ananena nao, Mukani kudziko lonse lapansi, lalikirani Uthenga Wabwino kwa olengedwa onse.


Pakuti kulibe kusiyana Myuda ndi Mgriki; pakuti Yemweyo ali Ambuye wa onse, nawachitira zolemera onse amene aitana pa Iye;


Koma ine nditi, Sanamva iwo kodi! Indetu, Liu lao linatulukira kudziko lonse lapansi, ndi maneno ao ku malekezero a dziko lokhalamo anthu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa