Luka 3:18 - Buku Lopatulika18 Choteretu iye anauza anthu Uthenga Wabwino ndi kuwadandaulira zinthu zina zambiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Choteretu iye anauza anthu Uthenga Wabwino ndi kuwadandaulira zinthu zina zambiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Yohane ankalalikira anthu Uthenga Wabwino pakuŵalangiza motero, ndiponso mwa njira zina zambiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Ndipo ndi mawu ena ambiri, Yohane anawachenjeza anthu ndi kuwalalikira Uthenga Wabwino. Onani mutuwo |