Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 24:51 - Buku Lopatulika

51 Ndipo kunali, pakuwadalitsa Iye analekana nao, natengedwa kunka Kumwamba.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

51 Ndipo kunali, pakuwadalitsa Iye analekana nao, natengedwa kunka Kumwamba.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

51 Akuŵadalitsa choncho, adalekana nawo, natengedwa kupita Kumwamba.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

51 Iye akuwadalitsa, anawasiya ndipo anatengedwa kupita kumwamba.

Onani mutuwo Koperani




Luka 24:51
9 Mawu Ofanana  

Ndipo kunachitika, akali chiyendere ndi kukambirana, taonani, anaoneka galeta wamoto ndi akavalo amoto, nawalekanitsa awiriwa; Eliya nakwera kumwamba ndi kamvulumvulu.


Pamenepo Ambuye Yesu, atatha kulankhula nao, analandiridwa Kumwamba, nakhala padzanja lamanja la Mulungu.


Ndipo anatuluka nao kufikira ku Betaniya; nakweza manja ake, nawadalitsa.


Ndipo anamlambira Iye, nabwera ku Yerusalemu ndi chimwemwe chachikulu;


Yesu ananena naye, Usandikhudze, pakuti sinditha kukwera kwa Atate; koma pita kwa abale anga, ukati kwa iwo, Ndikwera kunka kwa Atate wanga, ndi Mulungu wanu.


Ndipo m'mene adanena izi, ali chipenyerere iwo, ananyamulidwa; ndipo mtambo unamlandira Iye kumchotsa kumaso kwao.


ameneyo, pokhala ali chinyezimiro cha ulemerero wake, ndi chizindikiro chenicheni cha chikhalidwe chake, nanyamula zonse ndi mau a mphamvu yake, m'mene adachita chiyeretso cha zoipa, anakhala padzanja lamanja la Ukulu mu Mwamba,


Popeza tsono tili naye Mkulu wa ansembe wamkulu, wopyoza miyamba, Yesu mwana wa Mulungu, tigwiritsitse chivomerezo chathu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa