Luka 24:51 - Buku Lopatulika51 Ndipo kunali, pakuwadalitsa Iye analekana nao, natengedwa kunka Kumwamba. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201451 Ndipo kunali, pakuwadalitsa Iye analekana nao, natengedwa kunka Kumwamba. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa51 Akuŵadalitsa choncho, adalekana nawo, natengedwa kupita Kumwamba. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero51 Iye akuwadalitsa, anawasiya ndipo anatengedwa kupita kumwamba. Onani mutuwo |