Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Luka 24:50 - Buku Lopatulika

50 Ndipo anatuluka nao kufikira ku Betaniya; nakweza manja ake, nawadalitsa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

50 Ndipo anatuluka nao kufikira ku Betaniya; nakweza manja ake, nawadalitsa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

50 Atatero Yesu adaŵatsogolera kuchokera mumzindamo mpaka ku mudzi wa Betaniya. Kumeneko adakweza manja ake naŵadalitsa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

50 Iye atawatengera kunja kwa mzindawo mpaka ku Betaniya, anakweza manja ake ndi kuwadalitsa.

Onani mutuwo Koperani




Luka 24:50
15 Mawu Ofanana  

nundikonzere ine chakudya chokolera chonga chomwe ndichikonda ine, nudze nacho kwa ine kuti ndidzadye; kuti moyo wanga ukadalitse iwe ndisanafe.


Ndipo Yosefe anati kwa atate wake, Amenewa ndi ana anga, amene Mulungu wandipatsa ine pano. Ndipo iye anati, Udze naotu kwa ine, ndipo ndidzawadalitsa.


Awa onse ndiwo mafuko khumi ndi awiri a Israele: izo ndizo zomwe ananena kwa iwo atate wao nawadalitsa; yense monga mdalitso wake anawadalitsa.


Ndipo Aroni anakweza dzanja lake kulozera anthu, nawadalitsa; natsika kuja anapereka nsembe yauchimo, ndi nsembe yopsereza, ndi nsembe zoyamika.


Ndipo Iye anawasiya, natuluka m'mzinda, napita ku Betaniya, nagona kumeneko.


Ndipo Iye anatiyangata, natidalitsa, ndi kuika manja ake pa ito.


Ndipo pamene iwo anayandikira ku Yerusalemu, ku Betefage ndi Betaniya, paphiri la Azitona, anatuma awiri a ophunzira ake,


Ndipo kunali, pakuwadalitsa Iye analekana nao, natengedwa kunka Kumwamba.


Pamenepo anabwera ku Yerusalemu kuchokera kuphiri lonenedwa la Azitona, limene liyandikana ndi Yerusalemu, loyendako tsiku la Sabata.


Ndipo m'mene adanena izi, ali chipenyerere iwo, ananyamulidwa; ndipo mtambo unamlandira Iye kumchotsa kumaso kwao.


Chifukwa chake ndifuna kuti amunawo apemphere pamalo ponse, ndi kukweza manja oyera, opanda mkwiyo ndi makani.


Momwemo Yoswa anawadalitsa, nawauza amuke; ndipo anamuka ku mahema ao.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa