Luka 24:50 - Buku Lopatulika50 Ndipo anatuluka nao kufikira ku Betaniya; nakweza manja ake, nawadalitsa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201450 Ndipo anatuluka nao kufikira ku Betaniya; nakweza manja ake, nawadalitsa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa50 Atatero Yesu adaŵatsogolera kuchokera mumzindamo mpaka ku mudzi wa Betaniya. Kumeneko adakweza manja ake naŵadalitsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero50 Iye atawatengera kunja kwa mzindawo mpaka ku Betaniya, anakweza manja ake ndi kuwadalitsa. Onani mutuwo |