Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 24:43 - Buku Lopatulika

43 Ndipo anachitenga, nachidya pamaso pao.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

43 Ndipo anachitenga, nachidya pamaso pao.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

43 Iye atalandira nsombayo, adaidya iwo akuwona.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

43 Iye anakatenga ndi kukadya iwo akuona.

Onani mutuwo Koperani




Luka 24:43
2 Mawu Ofanana  

Ndipo anampatsa Iye chidutsu cha nsomba yokazinga.


si kwa anthu onse ai, koma kwa mboni zosankhidwiratu ndi Mulungu, ndiwo ife amene tinadya ndi kumwa naye pamodzi, atauka iye kwa akufa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa