Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 24:20 - Buku Lopatulika

20 ndi kuti ansembe aakulu ndi akulu athu anampereka Iye ku chiweruziro cha imfa, nampachika Iye pamtanda.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

20 ndi kuti ansembe aakulu ndi akulu athu anampereka Iye ku chiweruziro cha imfa, nampachika Iye pamtanda.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

20 Akulu a ansembe ndi akulu athu ena adampereka kuti azengedwe mlandu ndi kuphedwa, ndipo adampachika pa mtanda.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

20 Akulu a ansembe ndi oweruza anamupereka Iye kuti aphedwe, ndipo anamupachika Iye;

Onani mutuwo Koperani




Luka 24:20
14 Mawu Ofanana  

Njoka inu, obadwa inu a mamba, mudzatha bwanji kuthawa kulanga kwake kwa Gehena?


Koma ansembe aakulu ndi akulu anapangira anthu kuti apemphe Barabasi, koma kuti aononge Yesu.


Ndipo pomwepo mamawa anakhala upo ansembe aakulu, ndi akulu a anthu, ndi alembi, ndi akulu a milandu onse, namanga Yesu, namtenga, nampereka kwa Pilato.


Ndipo pamene kunacha, bungwe la akulu a anthu linasonkhana, ndiwo ansembe aakulu ndi alembi; ndipo anapita naye kubwalo lao,


Ndipo Pilato anaitana ansembe aakulu, ndi akulu, ndi anthu, asonkhane,


ameneyo, woperekedwa ndi uphungu woikidwa ndi kudziwiratu kwa Mulungu, inu mwampachika ndi kumupha ndi manja a anthu osaweruzika;


amene adaphanso Ambuye Yesu, ndi aneneri, natilondalonda ife, ndipo sakondweretsa Mulungu, natsutsana nao anthu onse;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa