Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 24:17 - Buku Lopatulika

17 Ndipo anati kwa iwo, Mau awa ndi otani mulandizanawo poyendayenda? Ndipo anaima ndi nkhope zao zachisoni.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

17 Ndipo anati kwa iwo, Mau awa ndi otani mulandizanawo poyendayenda? Ndipo anaima ndi nkhope zao zachisoni.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

17 Tsono Yesu adaŵafunsa kuti, “Kodi mukunka mukukambirana zotani panjira pano?” Apo iwo adaima, nkhope zao zili zakugwa ndi chisoni,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

17 Iye anawafunsa kuti, “Kodi mukukambirana zotani mʼnjira muno?” Iwo anayima ndi nkhope zakugwa.

Onani mutuwo Koperani




Luka 24:17
5 Mawu Ofanana  

Koma maso ao anagwidwa kuti asamzindikire Iye.


Ndipo mmodzi wa iwo, dzina lake Kleopa, anayankha nati kwa Iye, Kodi iwe wekha ndiwe mlendo mu Yerusalemu ndi wosazindikira zidachitikazi masiku omwe ano?


Koma chifukwa ndalankhula izi ndi inu chisoni chadzala mumtima mwanu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa