Luka 24:14 - Buku Lopatulika14 Ndipo iwowa anakambirana nkhani za izi zonse zidachitika. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Ndipo iwowa anakambirana nkhani za izi zonse zidachitika. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Ankakambirana za zonse zimene zidaachitika. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Iwo ankayankhulana za zonse zimene zinachitikazo. Onani mutuwo |