Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 24:14 - Buku Lopatulika

14 Ndipo iwowa anakambirana nkhani za izi zonse zidachitika.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

14 Ndipo iwowa anakambirana nkhani za izi zonse zidachitika.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

14 Ankakambirana za zonse zimene zidaachitika.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

14 Iwo ankayankhulana za zonse zimene zinachitikazo.

Onani mutuwo Koperani




Luka 24:14
5 Mawu Ofanana  

Pakuti Ine Yehova sindisinthika, chifukwa chake inu ana a Yakobo simunathedwe.


Ndipo taonani, awiri a mwa iwo analikupita tsiku lomwelo kumudzi dzina lake Emausi, wosiyana ndi Yerusalemu mastadiya makumi asanu ndi limodzi.


Ndipo kunali m'kukambirana kwao ndi kufunsana, Yesu mwini anayandikira, natsagana nao.


Munthu wabwino atulutsa zabwino m'chuma chokoma cha mtima wake; ndi munthu woipa atulutsa zoipa m'choipa chake: pakuti m'kamwa mwake mungolankhula mwa kuchuluka kwa mtima wake.


ndipo muziwaphunzitsa mwachangu kwa ana anu, ndi kuwalankhula awa pokhala pansi m'nyumba zanu, ndi poyenda inu panjira, ndi pogona inu pansi, ndi pouka inu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa