Luka 23:6 - Buku Lopatulika6 Koma pamene Pilato anamva, anafunsa ngati munthuyu ali Mgalileya. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Koma pamene Pilato anamva, anafunsa ngati munthuyu ali Mgalileya. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Pamene Pilato adamva zimenezi, adaŵafunsa kuti, “Kodi munthuyu ndi wa ku Galileya?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Pakumva zimenezi, Pilato anafunsa ngati munthuyo ndi Mgalileya. Onani mutuwo |