Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 21:32 - Buku Lopatulika

32 Indetu ndinena ndinu, Mbadwo uno sudzapitirira, kufikira zonse zitachitika.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

32 Indetu ndinena ndinu, Mbadwo uno sudzapitirira, kufikira zonse zitachitika.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

32 Ndithu ndikunenetsa kuti zonsezi zidzaoneka anthu a mbadwo unoŵa asanamwalire onse.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

32 “Zoonadi, Ine ndikukuwuzani kuti mʼbado uno sudzatha mpaka zinthu zonsezi zitachitika.

Onani mutuwo Koperani




Luka 21:32
7 Mawu Ofanana  

Indetu ndinena kwa inu, kuti alipo ena a iwo aima pano sadzalawa ndithu imfa, kufikira adzaona Mwana wa Munthu atadza mu ufumu wake.


Indetu ndinena kwa inu, Zinthu zonse izi zidzafika pa mbadwo uwu wamakono.


Indetu ndinena kwa inu, mbadwo uwu sudzatha kuchoka, kufikira zinthu zonsezi zidzachitidwa.


Indetu ndinena ndi inu, Mbadwo uno sudzapita kufikira zinthu izi zonse zitachitika.


Inde chotero inunso, pakuona zinthu izi zilikuchitika, zindikirani kuti Ufumu wa Mulungu uli pafupi.


Thambo ndi dziko lapansi zidzapita; koma mau anga sadzapita.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa