Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Luka 21:31 - Buku Lopatulika

31 Inde chotero inunso, pakuona zinthu izi zilikuchitika, zindikirani kuti Ufumu wa Mulungu uli pafupi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

31 Inde chotero inunso, pakuona zinthu izi zilikuchitika, zindikirani kuti Ufumu wa Mulungu uli pafupi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

31 Momwemonso, mukadzaona zija ndanenazi zikuchitika, mudzadziŵe kuti ufumu wa Mulungu uli pafupi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

31 Chimodzimodzinso, mukadzaona zinthu zonsezi, dziwani kuti ufumu wa Mulungu uli pafupi.

Onani mutuwo Koperani




Luka 21:31
7 Mawu Ofanana  

nanena, Tembenukani mitima; chifukwa Ufumu wa Kumwamba wayandikira.


Indetu ndinena ndinu, Mbadwo uno sudzapitirira, kufikira zonse zitachitika.


Pakuti katsala kanthawi kakang'onong'ono, ndipo wakudzayo adzafika, wosachedwa.


Musaipidwe wina ndi mnzake, abale, kuti mungaweruzidwe. Taonani, woweruza aima pakhomo.


Koma chitsiriziro cha zinthu zonse chili pafupi; chifukwa chake khalani anzeru, ndipo dikirani m'mapemphero;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa