Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 21:30 - Buku Lopatulika

30 pamene iphukira, muipenya nimuzindikira pa nokha kuti dzinja lili pafupi pomwepo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

30 pamene iphukira, muipenya nimuzindikira pa nokha kuti dzinja lili pafupi pomwepo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

30 Mukamaona kuti masamba akuphuka, mumadziŵa kuti chilimwe chayandikira kale.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

30 Ikamatulutsa masamba, mumakhoza kudzionera nokha ndi kudziwa kuti dzinja lili pafupi.

Onani mutuwo Koperani




Luka 21:30
4 Mawu Ofanana  

Koma phunzirani ndi mkuyu fanizo lake; pamene tsopano nthambi yake ili yanthete, niphuka masamba ake, muzindikira kuti dzinja liyandikira;


Ndipo inunso, pa nokha mulekeranji kuweruza kolungama?


Ndipo ananena nao fanizo; Onani mkuyu, ndi mitengo yonse:


Dziyeseni nokha, ngati muli m'chikhulupiriro, dzitsimikizeni nokha. Kapena simuzindikira kodi za inu nokha kuti Yesu Khristu ali mwa inu? Mukapanda kukhala osatsimikizidwa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa