Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 21:18 - Buku Lopatulika

18 Ndipo silidzaonongeka tsitsi limodzi la pamutu panu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

18 Ndipo silidzaonongeka tsitsi limodzi la pamutu panu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

18 Koma silidzatayikapo tsitsi lanu ndi limodzi lomwe.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

18 Koma palibe tsitsi limodzi la mʼmutu mwanu lidzawonongeke.

Onani mutuwo Koperani




Luka 21:18
7 Mawu Ofanana  

Nati iye, Mfumu mukumbukire Yehova Mulungu wanu kuti wolipsa mwazi asaonjeze kuononga, kuti angaononge mwana wanga. Niti iyo, Pali Yehova, palibe tsitsi limodzi la mwana wako lidzagwa pansi.


komatu inu, matsitsi onse a m'mutu mwanu awerengedwa.


komatu ngakhale matsitsi onse a pamutu panu awerengedwa. Musaopa, muposa mtengo wake wa mpheta zambiri.


Ndipo anthu onse adzadana ndi inu chifukwa cha dzina langa.


Momwemo ndikuchenjezani mutenge kanthu kakudya; pakuti kumeneku ndi kwa chipulumutso chanu; pakuti silidzatayika tsitsi la pamutu wa mmodzi wa inu.


Ndipo anthuwo ananena ndi Saulo, kodi Yonatani adzafa, amene anachititsa chipulumutso chachikulu ichi mu Israele? Musatero. Pali Yehova, palibe tsitsi limodzi la pamutu wake lidzagwa pansi, pakuti iye anagwirizana ndi Mulungu lero. Chomwecho anthuwo anapulumutsa Yonatani kuti angafe.


Ngakhale anauka anthu kukulondolani, ndi kufuna moyo wanu, koma moyo wa mbuye wanga udzamangika m'phukusi la amoyo lakukhala ndi Yehova Mulungu wanu; koma Iye adzaponya miyoyo ya adani anu kuwataya monga chotuluka m'choponyera mwala.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa