Luka 21:17 - Buku Lopatulika17 Ndipo anthu onse adzadana ndi inu chifukwa cha dzina langa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Ndipo anthu onse adzadana ndi inu chifukwa cha dzina langa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Anthu onse adzadana nanu chifukwa cha Ine. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Anthu onse adzakudani chifukwa cha Ine. Onani mutuwo |