Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 20:32 - Buku Lopatulika

32 Pomalizira anamwaliranso mkaziyo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

32 Pomalizira anamwaliranso mkaziyo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

32 Potsiriza pake mai uja nayenso adamwalira.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

32 Pa mapeto pake mkaziyo anafanso.

Onani mutuwo Koperani




Luka 20:32
6 Mawu Ofanana  

Mbadwo wina upita, mbadwo wina nufika; koma dziko lingokhalabe masiku onse.


Pakuti amoyo adziwa kuti tidzafa; koma akufa sadziwa kanthu bii, sadzalandira mphotho; pakuti angoiwalika.


ndi wachitatu anamtenga mkaziyo; ndipo choteronso asanu ndi awiri onse, sanasiye mwana, namwalira.


Potero m'kuuka iye adzakhala mkazi wa yani wa iwo? Pakuti asanu ndi awiriwo adamkwatira iye.


Ndipo popeza kwaikikatu kwa anthu kufa kamodzi, ndipo atafa, chiweruziro;


Ndiponso mbadwo uwu wonse unasonkhanidwa kuikidwa kwa makolo ao; nuuka mbadwo wina pambuyo pao; wosadziwa Yehova kapena ntchitoyi adaichitira Israele.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa