Luka 20:16 - Buku Lopatulika16 Iye adzafika nadzaononga olima munda aja, nadzapatsa munda kwa ena. Ndipo pamene iwo anamva, anati, Musatero iai! Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Iye adzafika nadzaononga olima munda aja, nadzapatsa munda kwa ena. Ndipo pamene iwo anamva, anati, Musatero iai! Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Ndithu adzabwera naŵapha alimiwo, munda uja nkuubwereka ena.” Anthu aja atamva zimenezi adati, “Ai, msatero.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Iye adzabwera ndi kupha alimi aja ndi kupereka mundawo kwa ena.” Pamene anthu anamva izi, anati, “Musatero ayi.” Onani mutuwo |