Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Luka 20:15 - Buku Lopatulika

15 Ndipo anamponya kunja kwa mundawo, namupha. Pamenepo mwini munda wampesawo adzawachitira chiyani?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

15 Ndipo anamponya kunja kwa mundawo, namupha. Pamenepo mwini munda wamphesawo adzawachitira chiyani?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

15 Tsono adamuponya kunja kwa mundawo, namupha. Kodi mwini munda wamphesa uja adzaŵatani alimi aja?

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

15 Ndipo anamuponya kunja kwa mundawo ndi kumupha. “Nanga tsono mwini munda wamphesayo adzawatani anthuwa?

Onani mutuwo Koperani




Luka 20:15
5 Mawu Ofanana  

Koma olimawo, pamene anamuona, anauzana wina ndi mnzake, nati, Uyu ndiye wolowa nyumba; tiyeni timuphe, kuti cholowa chake chikhale chathu.


Iye adzafika nadzaononga olima munda aja, nadzapatsa munda kwa ena. Ndipo pamene iwo anamva, anati, Musatero iai!


Mwa ichi Yesunso, kuti akayeretse anthuwo mwa mwazi wa Iye yekha, adamva chowawa kunja kwa chipata.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa