Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 2:8 - Buku Lopatulika

8 Ndipo panali abusa m'dziko lomwelo, okhala kubusa ndi kuyang'anira zoweta zao usiku.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Ndipo panali abusa m'dziko lomwelo, okhala kubusa ndi kuyang'anira zoweta zao usiku.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Ku dera lomwelo kunali abusa amene ankalonda zoŵeta zao ku dambo usiku.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Ndipo kunali abusa amene amakhala ku dera lomwelo, kuyangʼanira ziweto zawo usiku.

Onani mutuwo Koperani




Luka 2:8
8 Mawu Ofanana  

Pali Ine, ati Ambuye Yehova, zedi, popeza nkhosa zanga zinakhala nyama, ndi nkhosa zanga zinakhala chakudya cha zilombo zonse zakuthengo, chifukwa kunalibe mbusa, ndi abusa anga sanafunefune nkhosa zanga, koma abusawo anadzidyetsa okha, osadyetsa nkhosa zanga;


Ndipo iye anabala mwana wake wamwamuna woyamba; namkulunga Iye m'nsalu, namgoneka modyera ng'ombe, chifukwa kuti anasowa malo m'nyumba ya alendo.


Ndipo mngelo wa Ambuye anaimirira pa awo, ndi kuwala kwa Ambuye kunawaunikira kozungulira: ndipo anaopa ndi mantha aakulu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa