Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 2:45 - Buku Lopatulika

45 ndipo pamene sanampeze, anabwera ku Yerusalemu, namfunafuna Iye.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

45 ndipo pamene sanampeze, anabwera ku Yerusalemu, namfunafuna Iye.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

45 Ataona kuti sakumpeza, adabwerera ku Yerusalemu akumufunafuna ndithu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

45 Atalephera kumupeza, anabwerera ku Yerusalemu kukamufuna.

Onani mutuwo Koperani




Luka 2:45
2 Mawu Ofanana  

koma iwo anayesa kuti Iye ali m'chipiringu cha ulendo, nayenda ulendo wa tsiku limodzi; ndipo anayamba kumfunafuna Iye mwa abale ao ndi mwa anansi ao;


Ndipo pakupita masiku atatu, anampeza Iye mu Kachisi, analikukhala pakati pa aphunzitsi, namva iwo, nawafunsanso mafunso.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa