Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 2:33 - Buku Lopatulika

33 Ndipo atate ndi amake anali kuzizwa ndi zinthu zolankhulidwa za Iye.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

33 Ndipo atate ndi amake anali kuzizwa ndi zinthu zolankhulidwa za Iye.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

33 Atate ndi amai a mwanayo ankangodabwa nazo zimene Simeoni ankanena za mwanayo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

33 Abambo ndi amayi a Mwanayo anadabwa chifukwa cha zimene zinanenedwa za Iye.

Onani mutuwo Koperani




Luka 2:33
8 Mawu Ofanana  

Taonani, ine ndi ana amene Yehova wandipatsa ine, tili zizindikiro ndi zodabwitsa mwa Israele, kuchokera kwa Yehova wa makamu, amene akhala m'phiri la Ziyoni.


Pamene Iye anali chilankhulire ndi makamu, onani, amake ndi abale ake anaima panja, nafuna kulankhula naye.


Ndipo pakumva ichi, Yesu anazizwa, nati kwa iwo akumtsata, Indetu ndinena kwa inu, ngakhale mwa Israele, sindinapeze chikhulupiriro chotere.


Ndipo anthu onse amene anamva anazizwa ndi zinthu abusa adalankhula nao.


Ndipo m'mene anamuona Iye, anadabwa; ndipo amake anati kwa Iye, Mwanawe, wachitiranji ife chotero; taona, atate wako ndi ine tinalikufunafuna Iwe ndi kuda nkhawa.


Ndipo sanakhoze kugwira mauwo pamaso pa anthu; ndipo anazizwa ndi kuyankha kwake, nakhala chete.


Ndipo onse anadabwa pa ukulu wake wa Mulungu. Koma pamene onse analikuzizwa ndi zonse anazichita, Iye anati kwa ophunzira ake,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa