Luka 2:33 - Buku Lopatulika33 Ndipo atate ndi amake anali kuzizwa ndi zinthu zolankhulidwa za Iye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201433 Ndipo atate ndi amake anali kuzizwa ndi zinthu zolankhulidwa za Iye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa33 Atate ndi amai a mwanayo ankangodabwa nazo zimene Simeoni ankanena za mwanayo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero33 Abambo ndi amayi a Mwanayo anadabwa chifukwa cha zimene zinanenedwa za Iye. Onani mutuwo |