Luka 2:32 - Buku Lopatulika32 kuunika kukhale chivumbulutso cha kwa anthu a mitundu, ndi ulemerero wa anthu anu Israele. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201432 kuunika kukhale chivumbulutso cha kwa anthu a mitundu, ndi ulemerero wa anthu anu Israele. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa32 Mwapereka kuŵala kodzaunikira anthu a mitundu ina, kodzakhala ulemerero wa anthu anu Aisraele.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero32 kuwala kowunikira anthu a mitundu ina ndi kwa ulemerero kwa anthu anu Aisraeli.” Onani mutuwo |