Luka 2:29 - Buku Lopatulika29 Tsopano, Ambuye, monga mwa mau anu aja, lolani ine, kapolo wanu, ndichoke mumtendere; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201429 Tsopano, Ambuye, monga mwa mau anu aja, lolani ine, kapolo wanu, ndichoke mumtendere; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa29 “Ambuye, tsopano mundilole ine mtumiki wanu, ndipite ndi mtendere, pakuti mwachitadi zija mudaalonjezazi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero29 “Ambuye waulamuliro, monga munalonjeza, tsopano lolani kuti mtumiki wanu apite mu mtendere. Onani mutuwo |