Luka 2:28 - Buku Lopatulika28 pomwepo iye anamlandira Iye m'manja mwake, nalemekeza Mulungu, nati, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201428 pomwepo iye anamlandira Iye m'manja mwake, nalemekeza Mulungu, nati, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa28 Pamenepo Simeoni adalandira mwanayo m'manja mwake, nayamba kutamanda Mulungu ndi mau akuti, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero28 Simeoni anamunyamula mʼmanja mwake nayamika Mulungu, nati: Onani mutuwo |