Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 19:34 - Buku Lopatulika

34 Ndipo anati, Ambuye amfuna iye.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

34 Ndipo anati, Ambuye amfuna iye.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

34 Iwo adati, “Ambuye ali naye ntchito.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

34 Iwo anayankha kuti, “Ambuye akumufuna.”

Onani mutuwo Koperani




Luka 19:34
6 Mawu Ofanana  

Kondwera kwambiri, mwana wamkazi wa Ziyoni; fuula mwana wamkazi wa Yerusalemu; taona, Mfumu yako ikudza kwa iwe; ndiye wolungama, ndi mwini chipulumutso; wofatsa ndi wokwera pabulu, ndi mwana wamphongo wa bulu.


Ndipo pamene anamasula mwana wa bulu, eni ake anati kwa iwo, Mumasuliranji mwana wa bulu?


Ndipo anadza naye kwa Yesu; ndipo anayalika zovala zao pa mwana wa buluyo, nakwezapo Yesu.


Ngati anawatcha milungu iwo amene mau a Mulungu anawadzera (ndipo cholemba sichingathe kuthyoka),


Izi sanazidziwe ophunzira ake poyamba; koma pamene Yesu analemekezedwa, pamenepo anakumbukira kuti izi zinalembedwa za Iye, ndi kuti adamchitira Iye izi.


Pakuti mudziwa chisomo cha Ambuye wathu Yesu Khristu, kuti, chifukwa cha inu anakhala wosauka, angakhale anali wolemera, kuti inu ndi kusauka kwake mukakhale olemera.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa