Luka 19:35 - Buku Lopatulika35 Ndipo anadza naye kwa Yesu; ndipo anayalika zovala zao pa mwana wa buluyo, nakwezapo Yesu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201435 Ndipo anadza naye kwa Yesu; ndipo anayalika zovala zao pa mwana wa buluyo, nakwezapo Yesu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa35 Tsono adapita naye kwa Yesu, nayamba kuyala zovala zao pa buluyo, nakwezapo Yesu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero35 Iwo anabweretsa buluyo kwa Yesu, naponya zovala zawo pa bulupo ndi kumukwezapo Yesu. Onani mutuwo |