Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Luka 19:35 - Buku Lopatulika

35 Ndipo anadza naye kwa Yesu; ndipo anayalika zovala zao pa mwana wa buluyo, nakwezapo Yesu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

35 Ndipo anadza naye kwa Yesu; ndipo anayalika zovala zao pa mwana wa buluyo, nakwezapo Yesu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

35 Tsono adapita naye kwa Yesu, nayamba kuyala zovala zao pa buluyo, nakwezapo Yesu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

35 Iwo anabweretsa buluyo kwa Yesu, naponya zovala zawo pa bulupo ndi kumukwezapo Yesu.

Onani mutuwo Koperani




Luka 19:35
9 Mawu Ofanana  

Nafulumira iwo, nagwira yense chofunda chake, nachiyala pokhala iye pachiunda, naomba lipenga, nati, Yehu ndiye mfumu.


Ndipo ichi chinatero, kuti chikachitidwe chonenedwa ndi mneneri kuti,


nabwera ndi bulu ndi mwana wake, naika pa iwo zovala zao, nakhala Iye pamenepo.


Ndipo anati, Ambuye amfuna iye.


Ndipo pakupita Iye, anayala zovala zao m'njira.


M'mawa mwake khamu lalikulu la anthu amene adadza kuchikondwerero, pakumva kuti Yesu alinkudza ku Yerusalemu,


Koma Yesu, m'mene adapeza kabulu anakhala pamenepo; monga mulembedwa:


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa