Luka 19:23 - Buku Lopatulika23 ndipo sunapereke bwanji ndalama yanga pokongoletsa, ndipo ine pakudza ndikadaitenga ndi phindu lake? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 ndipo sunapereka bwanji ndalama yanga pokongoletsa, ndipo ine pakudza ndikadaitenga ndi phindu lake? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Nanga bwanji osaiika ku banki ndalama yangayo, kuti ine pobwera ndiilandire pamodzi ndi chiwongoladzanja chake?’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Nanga nʼchifukwa chiyani sunasungitse ndalama yanga, kuti ine pobwera, ndidzayitenge ndi chiwongoladzanja?’ Onani mutuwo |