Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Luka 19:24 - Buku Lopatulika

24 Ndipo anati kwa iwo akuimirirapo, Mchotsereni minayo, nimuipatse kwa iye wakukhala nazo mina khumi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

24 Ndipo anati kwa iwo akuimirirapo, Mchotsereni minayo, nimuipatse kwa iye wakukhala nazo mina khumi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

24 Atatero adauza anthu amene anali pomwepo kuti, ‘Mlandeni ndalamayi muipereke kwa amene ali ndi ndalama makumi khumiyo.’

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

24 “Ndipo iye anawuza amene anayimirira pafupi kuti, ‘Tengani ndalama yake ndi kumupatsa amene ali ndi ndalama khumiyo!’ ”

Onani mutuwo Koperani




Luka 19:24
5 Mawu Ofanana  

Koma Mulungu anati kwa iye, Wopusa iwe, usiku womwe uno udzafunidwa moyo wako; ndipo zinthu zimene unazikonza zidzakhala za yani?


Ndipo anamuitana, nati kwa iye, Ichi ndi chiyani ndikumva za iwe? Undiwerengere za ukapitao wako; pakuti sungathe kukhalabe kapitao.


Ndipo anaitana akapolo ake khumi, nawapatsa iwo ndalama khumi za mina, nati kwaiwo, Chita nazoni malonda kufikira ndibweranso.


ndipo sunapereke bwanji ndalama yanga pokongoletsa, ndipo ine pakudza ndikadaitenga ndi phindu lake?


Ndipo anati kwa iye, Mbuye, ali nazo mina khumi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa