Luka 19:21 - Buku Lopatulika21 pakuti ndinakuopani, popeza inu ndinu munthu wouma mtima: munyamula chimene simunachiike pansi, mututa chimene simunachifese. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 pakuti ndinakuopani, popeza inu ndinu munthu wouma mtima: munyamula chimene simunachiika pansi, mututa chimene simunachifesa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Ndinkakuwopani, popeza kuti ndinu munthu wankhwidzi. Mumalonjerera zimene simudaikize, ndiponso mumakolola zimene simudabzale.’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Ine ndimakuopani, chifukwa ndinu munthu wowuma mtima. Inu mumatenga chimene simunachiyike ndi kukolola chimene simunadzale.’ Onani mutuwo |