Luka 19:20 - Buku Lopatulika20 Ndipo wina anadza, nanena, Mbuye, taonani, siyi mina yanu, ndaisunga m'kansalu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Ndipo wina anadza, nanena, Mbuye, taonani, siyi mina yanu, ndaisunga m'kansalu; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Koma wina adadza nati, ‘Ambuye, nayi ndalama yanu ija. Ndidaaimanga pa kansalu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 “Kenaka wantchito wina anabwera ndipo anati, ‘Bwana, ndalama yanu nayi; ine ndinayibisa ndi kuyisunga mʼkansalu. Onani mutuwo |