Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 19:2 - Buku Lopatulika

2 Ndipo taonani, mwamuna wotchedwa dzina lake Zakeyo; ndipo iye anali mkulu wa amisonkho, nali wachuma.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Ndipo taonani, mwamuna wotchedwa dzina lake Zakeyo; ndipo iye anali mkulu wa amisonkho, nali wachuma.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 Kudafika munthu wina, dzina lake Zakeyo. Iyeyo anali mkulu wa okhometsa msonkho, ndipo anali wolemera.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 Kunali munthu kumeneko dzina lake Zakeyu; iye anali mkulu wa wolandira msonkho ndipo anali wolemera.

Onani mutuwo Koperani




Luka 19:2
6 Mawu Ofanana  

Filipo, ndi Bartolomeo; Tomasi, ndi Mateyu wamsonkho yo; Yakobo mwana wa Alifeyo, ndi Tadeyo;


Ndipo analowa, napyola pa Yeriko.


Ndipo anafuna kuona Yesu ndiye uti, ndipo sanathe, chifukwa cha khamulo, pakuti anali wamfupi msinkhu.


Ndipo m'mene anadza pamalopo Yesu anakweza maso nati kwa iye, Zakeyo, fulumira, nutsike; pakuti lero ndiyenera kukhala m'nyumba mwako.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa