Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 19:18 - Buku Lopatulika

18 Ndipo anadza wachiwiri, nanena, Mbuye, mina yanu yapindula mina zisanu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

18 Ndipo anadza wachiwiri, nanena, Mbuye, mina yanu yapindula mina zisanu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

18 Wachiŵiri adadza nati, ‘Ambuye, ndalama yanu ija idapindula ndalama makumi asanu.’

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

18 “Wachiwiri anabwera ndipo anati, ‘Bwana, ndalama zanu zapindula zisanu zina.’

Onani mutuwo Koperani




Luka 19:18
7 Mawu Ofanana  

Ndipo iye amene afesedwa pa nthaka yabwino, uyu ndiye wakumva mau nawadziwitsa; amene abaladi zipatso, nazifitsa, ena za makumi khumi, ena za makumi asanu ndi limodzi, ena za makumi atatu.


Ndipo wa matalente awiriwo anadzanso, nati, Mbuye, munandipatsa ine matalente awiri; onani, ndapindulapo matalente ena awiri.


Ndipo iwo ofesedwa pa nthaka yabwino ndiwo oterewa akumva mau, nawalandira, nabala zipatso zakupindula makumi atatu, ndi makumi asanu ndi limodzi, ndi makumi khumi.


Ndipo anaitana akapolo ake khumi, nawapatsa iwo ndalama khumi za mina, nati kwaiwo, Chita nazoni malonda kufikira ndibweranso.


Ndipo anati kwa iye, Chabwino, kapolo wabwino iwe; popeza unakhala wokhulupirika m'chaching'onong'ono, khala nao ulamuliro pa mizinda khumi.


Ndipo anati kwa iyenso, Khala iwenso woweruza mizinda isanu.


Pakuti ngati chivomerezocho chili pomwepo, munthu alandiridwa monga momwe ali nacho, si monga chimsowa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa