Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Luka 19:19 - Buku Lopatulika

19 Ndipo anati kwa iyenso, Khala iwenso woweruza mizinda isanu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

19 Ndipo anati kwa iyenso, Khala iwenso woweruza midzi isanu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

19 Iyenso mbuye wake adamuuza kuti, ‘Iwe udzalamulira midzi isanu.’

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

19 “Bwana anayankha kuti, ‘Iwe lamulira mizinda isanu.’

Onani mutuwo Koperani




Luka 19:19
8 Mawu Ofanana  

Nenani za wolungama, kuti kudzamkomera iye; chifukwa oterowo adzadya zipatso za machitidwe ao.


Ndipo anadza wachiwiri, nanena, Mbuye, mina yanu yapindula mina zisanu.


Ndipo wina anadza, nanena, Mbuye, taonani, siyi mina yanu, ndaisunga m'kansalu;


Chifukwa chake, abale anga okondedwa, khalani okhazikika, osasunthika, akuchuluka mu ntchito ya Ambuye, nthawi zonse, podziwa kuti kuchititsa kwanu sikuli chabe mwa Ambuye.


Koma wookayo ndi wothirirayo ali amodzi; koma yense adzalandira mphotho yake ya iye yekha, monga mwa kuchititsa kwake kwa iye yekha.


Koma nditi ichi, kuti iye wakufesa mouma manja, mouma manjanso adzatuta. Ndipo iye wakufesa moolowa manja, moolowa manjanso adzatuta.


Mudzipenyerere nokha, kuti mungataye zimene tazichita, koma kuti mulandire mphotho yokwanira.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa