Luka 19:19 - Buku Lopatulika19 Ndipo anati kwa iyenso, Khala iwenso woweruza mizinda isanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Ndipo anati kwa iyenso, Khala iwenso woweruza midzi isanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Iyenso mbuye wake adamuuza kuti, ‘Iwe udzalamulira midzi isanu.’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 “Bwana anayankha kuti, ‘Iwe lamulira mizinda isanu.’ Onani mutuwo |