Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 18:41 - Buku Lopatulika

41 Ufuna ndikuchitire chiyani? Ndipo anati, Ambuye, kuti ndipenyenso.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

41 Ufuna ndikuchitire chiyani? Ndipo anati, Ambuye, kuti ndipenyenso.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

41 “Kodi ukufuna kuti ndikuchitire chiyani?” Iye adati, “Ambuye, ndikufuna kuti ndizipenyanso.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

41 “Kodi ukufuna kuti ndikuchitire chiyani?” Iye anayankha kuti, “Ambuye, ine ndifuna ndionenso.”

Onani mutuwo Koperani




Luka 18:41
6 Mawu Ofanana  

Ndipo Yesu anaima, nalamulira kuti abwere naye kwa Iye; ndipo m'mene adafika pafupi, anamfunsa iye,


Ndipo Yesu anati kwa iye, Penyanso: chikhulupiriro chako chakupulumutsa iwe.


Koma ngati tiyembekezera chimene sitichipenya, pomwepo tichilindirira ndi chipiriro.


Musadere nkhawa konse; komatu m'zonse ndi pemphero, ndi pembedzero, pamodzi ndi chiyamiko, zopempha zanu zidziwike kwa Mulungu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa