Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 18:40 - Buku Lopatulika

40 Ndipo Yesu anaima, nalamulira kuti abwere naye kwa Iye; ndipo m'mene adafika pafupi, anamfunsa iye,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

40 Ndipo Yesu anaima, nalamulira kuti abwere naye kwa Iye; ndipo m'mene adafika pafupi, anamfunsa iye,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

40 Yesu adaima nalamula kuti abwere naye kwa Iye. Atafika pafupi, Yesu adamufunsa kuti,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

40 Yesu anayima nalamula kuti abwere naye kwa Iye. Atabwera pafupi, Yesu anamufunsa kuti,

Onani mutuwo Koperani




Luka 18:40
4 Mawu Ofanana  

Ndipo iwo akutsogolera anamdzudzula iye, kuti akhale chete; koma iye anafuulitsa chifuulire, Mwana wa Davide, mundichitire chifundo.


Ufuna ndikuchitire chiyani? Ndipo anati, Ambuye, kuti ndipenyenso.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa